TEN MOUNTAIN SAFETY TIPS

  1. Never climb alone. A party of four is ideal.
  2. Choose a route according to the experience, ability and fitness of the group.
  3. Use a guidebook or go with someone who genuinely knows the way.
  4. Ensure that at least one member of the group has a fully charged cell phone.
  5. Always go prepared for bad weather
  6. Tell someone where you are going and stick to the plan
  7. Travel at the pace of the slowest member of the group
  8. Never split up and go in different directions
  9. Don’t push on into the unknown. If you get lost retrace your steps.
  10. If you are unsure of what to do find shelter especially from the wind and stay put.
  1. Musakwere Phiri nokha. Mukuyenera kukhala anthu anayi
  2. Sankhani njira yokwerera Phiri yomwe mungayithe malinga ndi luntha lanu komanso ndi mphamvu za gulu lanu.
  3. Gwirisani tnchito mabuku ofotokoza za momwe mungayendere mu Phiri kapena tengani munthu amene amalondorera anthu mu Phiri ndipo oziwa za Phiri kwambiri.
  4. Onesesani kuti m’modzi wagulu lanu ali ndi phone yo charger bwino.
  5. Nthawo zonse khalani okonzeka ukumana ndi nyengo yoyipa ngati yozizira ndipo nyamulani za mphepo.
  6. Uzani munthu ku malo komwe mukupita ndipo musasinthe.
  7. Musayende njira zosiyanasiyana pokwera Phiri, yendani limodzi ngati gulu.
  8. Yendani pa mlingo wa munthu woyenda pang’ono pang’ono pagulu lanulo
  9. Musapitirire pa njira yoti simukuyiziwa, mukasochera bwererani njira yomwe mwachokera.
  10. Ngati mwapezana ndi mphepo ya nkuntho, bisalani pamalo abwino ngati simukuziwa chochita.

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *